Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Hoseya 9:14 - Buku Lopatulika

14 Apatseni, Yehova; mudzapatsa chiyani? Muwapatse mimba yotayataya, ndi mawere ouma.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Apatseni, Yehova; mudzapatsa chiyani? Muwapatse mimba yotayataya, ndi mawere ouma.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Muŵapatse, Inu Chauta. Kodi mudzaŵapatse chiyani? Muŵapatse mimba yopita padera ndi maŵere ouma!

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Inu Yehova, muwapatse. Kodi mudzawapatsa chiyani? Apatseni mimba yomangopita padera ndi mawere owuma.

Onani mutuwo Koperani




Hoseya 9:14
11 Mawu Ofanana  

Ng'ombe yao yamphongo imakwera, yosakanika; ng'ombe yao yaikazi imaswa, yosapoloza.


M'dziko mwanu simudzakhala wakutaya mwana, kapena wosabala; ndidzakwaniritsa kuwerenga kwa masiku ako.


Kunena za Efuremu, ulemerero wao udzauluka ndi kuchoka ngati mbalame; sipadzakhala kubala, ndi kukhala ndi pakati, ndi kuima.


Efuremu, monga ndaona, akunga Tiro, wookedwa pokoma; koma Efuremu adzatulutsira ana ake wakuwaphera.


Efuremu wakanthidwa, muzu wao wauma, iwo sadzabala zipatso; inde ngakhale abala, koma ndidzapha zipatso zofunika za mimba yao.


Koma tsoka ali nalo iwo akukhala ndi pakati, ndi akuyamwitsa ana m'masiku awo!


Koma tsoka iwo akukhala ndi pakati, ndi akuyamwitsa ana masiku awo!


Koma tsoka iwo akukhala ndi pakati, ndi iwo akuyamwitsa ana masiku awo! Pakuti padzakhala chisauko chachikulu padziko, ndi mkwiyo pa anthu awa.


Chifukwa taonani masiku alinkudza, pamene adzati, Odala ali ouma ndi mimba yosabala, ndi mawere osayamwitsa.


Chifukwa chake ndiyesa kuti ichi ndi chokoma chifukwa cha chivuto cha nyengo ino, kuti nkwabwino kwa munthu kukhala monga ali.


Zidzakhala zotembereredwa zipatso za thupi lanu, ndi zipatso za nthaka yanu, zoswana za ng'ombe zanu, ndi zoswana za nkhosa zanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa