Hoseya 8:14 - Buku Lopatulika14 Pakuti Israele waiwala Mlengi wake, namanga akachisi; ndipo Yuda wachulukitsa mizinda yamalinga; koma ndidzatumizira mizinda yake moto, nudzatha nyumba zake zazikulu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Pakuti Israele waiwala Mlengi wake, namanga akachisi; ndipo Yuda wachulukitsa midzi yamalinga; koma ndidzatumizira midzi yake moto, nudzatha nyumba zake zazikulu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Aisraele adzimangira nyumba zikuluzikulu, kuiŵala Mlengi wao. Ayuda achulukitsa mizinda yamalinga. Koma Ine ndidzaponya moto pa mizinda yaoyo, ndipo motowo udzatentha nyumba zao zazikuluzo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Israeli wayiwala Mlengi wake ndipo wamanga nyumba zaufumu; Yuda wachulukitsa mizinda ya malinga. Koma Ine ndidzaponya moto pa mizinda yawoyo, moto umene udzatenthe malinga awo.” Onani mutuwo |