Hoseya 5:14 - Buku Lopatulika14 Pakuti ndidzakhala kwa Efuremu ngati mkango, ndi kwa nyumba ya Yuda ngati msona wa mkango; ndidzamwetula Ine ndi kuchoka; ndidzanyamula, ndipo palibe wakulanditsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Pakuti ndidzakhala kwa Efuremu ngati mkango, ndi kwa nyumba ya Yuda ngati msona wa mkango; ndidzamwetula Ine ndi kuchoka; ndidzanyamula, ndipo palibe wakulanditsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Ndidzalumphira Aefuremu ngati mkango, ndidzambwandira Ayuda ngati msona wa mkango. Ine mwini ndidzaŵakadzula nkuchokapo. Pamene ndizidzaŵaguza, palibe wina aliyense wotha kudzaŵalanditsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Pakuti Ine ndidzakhala ngati mkango kwa Efereimu. Ngati mkango wamphamvu kwa Yuda. Ndidzawakhadzula nʼkuchokapo; ndidzawatenga ndipo palibe amene adzawalanditse. Onani mutuwo |