Hoseya 5:13 - Buku Lopatulika13 Pamene Efuremu anaona nthenda yake, ndi Yuda bala lake, Efuremu anamuka kwa Asiriya, natumiza kwa mfumu Yarebu; koma iye sakhoza kukuchiritsani, kapena kupoletsa bala lanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Pamene Efuremu anaona nthenda yake, ndi Yuda bala lake, Efuremu anamuka kwa Asiriya, natumiza kwa mfumu Yarebu; koma iye sakhoza kukuchiritsani, kapena kupoletsa bala lanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 “Tsono anthu a ku Efuremu ataona kuti akudwala, ndipo Ayuda ataona kuti ali ndi mabala, Aefuremuwo adapita kwa Aasiriya, Ayuda natuma uthenga kwa mfumu yaikulu, kuti iŵathandize. Koma siingathe kuŵachiritsa kapena kupoletsa mabala ao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 “Efereimu ataona nthenda yake, ndi Yuda ataona zilonda zake, pamenepo Efereimu anatembenukira kwa Asiriya, ndipo anawatumizira mfumu yayikulu kudzawathandiza. Koma mfumuyo singathe kukuchizani, singathe kuchiritsa mabala anu. Onani mutuwo |