Hoseya 2:17 - Buku Lopatulika17 Pakuti ndidzachotsa maina a Abaala m'kamwa mwake; ndipo silidzakumbukikanso dzina lao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Pakuti ndidzachotsa maina a Abaala m'kamwa mwake; ndipo silidzakumbukikanso dzina lao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Ndidzamletsa kuti asatchulenso maina a Abaala, Ndithu anthu sadzatchulanso maina aowo popembedza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Ndidzachotsa mayina a Abaala pakamwa pake; sadzatchulanso mayina awo popemphera. Onani mutuwo |