Hoseya 14:7 - Buku Lopatulika7 Iwo okhala pansi pa mthunzi wake adzabwera, nadzatsitsimuka ngati tirigu, nadzaphuka ngati mpesa, chikumbukiro chake chidzanga vinyo wa Lebanoni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Iwo okhala pansi pa mthunzi wake adzabwera, nadzatsitsimuka ngati tirigu, nadzaphuka ngati mpesa, chikumbukiro chake chidzanga vinyo wa Lebanoni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Aisraele adzapezanso chitetezo mwa Ine. Adzakolola tirigu wambiri, adzachuluka ngati mphesa. Adzakhala otchuka ngati vinyo wa ku Lebanoni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Anthu adzakhalanso mu mthunzi wake. Iye adzakula bwino ngati tirigu. Adzachita maluwa ngati mphesa ndipo kutchuka kwake kudzakhala ngati vinyo wochokera ku Lebanoni. Onani mutuwo |