Hoseya 14:6 - Buku Lopatulika6 Nthambi zake zidzatambalala, ndi kukoma kwake kudzanga kwa mtengo wa azitona, ndi fungo lake ngati Lebanoni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Nthambi zake zidzatambalala, ndi kukoma kwake kudzanga kwa mtengo wa azitona, ndi fungo lake ngati Lebanoni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ziphukira zake zidzatambasukira kutali, adzakhala wokongola ngati mtengo wa olivi, adzakhala wonunkhira ngati mkungudza wa ku Lebanoni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 mphukira zake zidzakula. Kukongola kwake kudzakhala ngati mtengo wa olivi, kununkhira kwake ngati mkungudza wa ku Lebanoni. Onani mutuwo |