Hoseya 13:15 - Buku Lopatulika15 Chinkana abala mwa abale ake, mphepo ya kum'mawa idzafika, mphepo ya Yehova yokwera kuchokera kuchipululu; ndi gwero lake lidzaphwa, ndi kasupe wake adzauma, adzafunkha chuma cha akatundu onse ofunika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Chinkana abala mwa abale ake, mphepo ya kum'mawa idzafika, mphepo ya Yehova yokwera kuchokera kuchipululu; ndi gwero lake lidzaphwa, ndi kasupe wake adzauma, adzafunkha chuma cha akatundu onse ofunika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Ngakhale kuti Efuremu akondwe ngati bango, mphepo yakuvuma mphepo ya Chauta, idzakuntha kuchokera kuchipululu. Motero kasupe wake adzaphwa, ndipo chitsime chake chidzauma. Adani adzaononga chuma chake chamtengowapatali. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 ngakhale Efereimu akondwe pakati pa abale ake, mphepo ya kummawa yochokera kwa Yehova idzabwera, ikuwomba kuchokera ku chipululu. Kasupe wake adzaphwa ndipo chitsime chake chidzawuma. Chuma chake chonse chamtengowapatali chidzafunkhidwa ndipo chidzatengedwa. Onani mutuwo |