Hoseya 12:14 - Buku Lopatulika14 Efuremu wautsa mkwiyo wowawa, m'mwemo Iye adzamsiyira mwazi wake, ndi Ambuye wake adzambwezera chomtonza chake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Efuremu wautsa mkwiyo wowawa, m'mwemo Iye adzamsiyira mwazi wake, ndi Ambuye wake adzambwezera chomtonza chake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Koma Aefuremuwo adaputa mkwiyo wake, nchifukwa chake Chauta adzaŵalanga ndi imfa. Adzaŵalanga chifukwa adamchititsa manyazi kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Koma Efereimu wamukwiyitsa kwambiri. Nʼchifukwa chake Yehova adzawalanga ndi imfa. Adzawalanga chifukwa anamuchititsa manyazi kwambiri. Onani mutuwo |