Hoseya 10:14 - Buku Lopatulika14 Momwemo phokoso lidzaukira anthu ako, ndi malinga ako onse adzapasuka, monga Salimani anapasula Betaribele; tsiku la nkhondo amai anaphwanyika pamodzi ndi ana ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Momwemo phokoso lidzaukira anthu ako, ndi malinga ako onse adzapasuka, monga Salimani anapasula Betaribele; tsiku la nkhondo amai anaphwanyika pamodzi ndi ana ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 adani anu adzakuthirani nkhondo. Malinga anu onse adzaonongedwa monga momwe Salamani adaonongera Betaribele pa tsiku la nkhondo. Adaphwanya azimai pamodzi ndi ana omwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 phokoso lankhondo lidzamveka pakati pa anthu anga kotero kuti malinga anu onse adzawonongeka, monga momwe Salimani anawonongera Beti-Aribeli pa nthawi ya nkhondo; pamene anapha amayi pamodzi ndi ana awo omwe. Onani mutuwo |