Hoseya 10:13 - Buku Lopatulika13 Mwalima choipa, mwakolola chosalungama, mwadya zipatso za mabodza; pakuti watama njira yako ndi kuchuluka kwa anthu ako amphamvu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Mwalima choipa, mwakolola chosalungama, mwadya zipatso za mabodza; pakuti watama njira yako ndi kuchuluka kwa anthu ako amphamvu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Mudabzala zolakwa, ndipo mudakolola chilango chake. Mwadya zotsatira zake za mabodza. Chifukwa choti mwadalira magaleta anu, ndi kuchuluka kwa anthu anu a nkhondo, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Koma inu munadzala zolakwa, mwakolola zoyipa; mwadya chipatso cha chinyengo. Chifukwa mumadalira mphamvu zanu ndiponso ankhondo anu ochulukawo, Onani mutuwo |