Hagai 2:6 - Buku Lopatulika6 Pakuti atero Yehova wa makamu: Kamodzinso, katsala kanthawi, ndidzagwedeza miyamba ndi dziko lapansi, ndi nyanja, ndi mtunda womwe; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Pakuti atero Yehova wa makamu: Kamodzinso, katsala kanthawi, ndidzagwedeza miyamba ndi dziko lapansi, ndi nyanja, ndi mtunda womwe; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 “Zimene ndikunena Ine Chauta Wamphamvuzonse ndi izi: Patapita nthaŵi pang'ono, ndidzagwedeza mlengalenga ndi dziko lapansi, nyanja ndi mtunda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 “Yehova Wamphamvuzonse akuti, ‘Pakapita nthawi pangʼono ndidzagwedezanso thambo ndi dziko lapansi, nyanja ndi mtunda. Onani mutuwo |