Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Hagai 2:11 - Buku Lopatulika

11 Atero Yehova wa makamu: Funsatu ansembe za chilamulo, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Atero Yehova wa makamu: Funsatu ansembe za chilamulo, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 “Zimene ndikunena Ine Chauta Wamphamvuzonse ndi izi: Mupemphe ansembe kuti agamule nkhani iyi:

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 “Yehova Wamphamvuzonse akuti, ‘Funsa ansembe za zimene lamulo likunena:

Onani mutuwo Koperani




Hagai 2:11
7 Mawu Ofanana  

Ansembe ake achitira choipa chilamulo changa, nadetsa zopatulika zanga, sasiyanitsa pakati pa zopatulika ndi zinthu wamba, ndipo sazindikiritsa anthu pakati pa zodetsa ndi zoyera, nabisira masabata anga maso ao; ndipo Ine ndidetsedwa pakati pao.


Pakuti milomo ya wansembe iyenera kusunga chidziwitso, ndi anthu ayenera kufunafuna chilamulo pakamwa pake; pakuti iye ndiye mthenga wa Yehova wa makamu.


Adzaphunzitsa Yakobo maweruzo anu, ndi Israele chilamulo chanu; adzaika chofukiza pamaso panu, ndi nsembe yopsereza yamphumphu paguwa la nsembe lanu.


wogwira mau okhulupirika monga mwa chiphunzitso, kuti akakhoze kuchenjeza m'chiphunzitso cholamitsa, ndi kutsutsa otsutsana naye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa