Hagai 2:11 - Buku Lopatulika11 Atero Yehova wa makamu: Funsatu ansembe za chilamulo, ndi kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Atero Yehova wa makamu: Funsatu ansembe za chilamulo, ndi kuti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 “Zimene ndikunena Ine Chauta Wamphamvuzonse ndi izi: Mupemphe ansembe kuti agamule nkhani iyi: Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 “Yehova Wamphamvuzonse akuti, ‘Funsa ansembe za zimene lamulo likunena: Onani mutuwo |