Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Hagai 2:10 - Buku Lopatulika

10 Tsiku la makumi awiri ndi anai la mwezi wachisanu ndi chinai, chaka chachiwiri cha Dariusi, mau a Yehova anadza mwa Hagai mneneri, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Tsiku la makumi awiri ndi anai la mwezi wachisanu ndi chinai, chaka chachiwiri cha Dariusi, mau a Yehova anadza mwa Hagai mneneri, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Chaka chachiŵiri cha ufumu wa Dariusi pa tsiku la 24 la mwezi wachisanu ndi chinai, Chauta adapatsa mneneri Hagai uthenga uwu wakuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Chaka chachiwiri cha Dariyo, pa tsiku la 24 la mwezi wachisanu ndi chinayi, Yehova anayankhula ndi mneneri Hagai kuti:

Onani mutuwo Koperani




Hagai 2:10
6 Mawu Ofanana  

Chaka chachiwiri cha mfumu Dariusi, mwezi wachisanu ndi chimodzi, mau a Yehova anadza mwa Hagai mneneri kwa Zerubabele mwana wa Sealatiele, chiwanga cha Yuda, ndi kwa Yoswa mwana wa Yehozadaki, mkulu wa ansembe, ndi kuti,


tsiku la makumi awiri ndi anai la mwezi, mwezi wachisanu ndi chimodzi, chaka chachiwiri cha mfumu Dariusi.


Musamalire, kuyambira lero ndi m'tsogolo, kuyambira tsiku la makumi awiri ndi chinai la mwezi wachisanu ndi chinai, kuyambira tsiku lija anamanga maziko a Kachisi wa Yehova, samalirani.


Ndipo mau a Yehova anadza nthawi yachiwiri kwa Hagai tsiku la makumi awiri la mwezi, ndi kuti,


Mwezi wachisanu ndi chitatu, chaka chachiwiri cha Dariusi, mau a Yehova anadza kwa Zekariya mwana wa Berekiya, mwana wa Ido mneneri, ndi kuti,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa