Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Hagai 1:7 - Buku Lopatulika

7 Atero Yehova wa makamu: Mtima wanu usamalire njira zanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Atero Yehova wa makamu: Mtima wanu usamalire njira zanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 “Nchifukwa chake Ine Chauta Wamphamvuzonse ndikunena kuti muganizeponso bwinotu pamenepa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Ganizirani bwino njira zanu.

Onani mutuwo Koperani




Hagai 1:7
8 Mawu Ofanana  

Pakuti pali langizo ndi langizo, langizo ndi langizo; lamulo ndi lamulo, lamulo ndi lamulo; kuno pang'ono, uko pang'ono.


Tisanthule ntiyese njira zathu ntibwerenso kwa Yehova.


Chifukwa chake tsono, atero Yehova wa makamu: Mtima wanu usamalire njira zanu.


Mwabzala zambiri, koma mututa pang'ono; mukudya, koma osakhuta; mukumwa, koma osakoledwa; mudziveka, koma palibe wofundidwa; ndi iye wolembedwa ntchito yakulipidwa alandirira kulipirako m'thumba lobooka.


Kwerani kudziko la mapiri, ndi kukwera nayo mitengo, nimumange nyumbayi; ndipo kudzandikomera, ndipo ndidzalemekezedwa, ati Yehova.


Ndipo tsono, samalirani, kuyambira lero ndi m'tsogolomo, kuti, kusanaikidwe mwala pamwala mu Kachisi wa Yehova,


Chotsalira, abale anga, kondwerani mwa Ambuye. Kulembera zomwezo kwa inu, sikundivuta ine, koma kwa inu kuli kukhazikitsa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa