Hagai 1:7 - Buku Lopatulika7 Atero Yehova wa makamu: Mtima wanu usamalire njira zanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Atero Yehova wa makamu: Mtima wanu usamalire njira zanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 “Nchifukwa chake Ine Chauta Wamphamvuzonse ndikunena kuti muganizeponso bwinotu pamenepa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Ganizirani bwino njira zanu. Onani mutuwo |