Hagai 1:5 - Buku Lopatulika5 Chifukwa chake tsono, atero Yehova wa makamu: Mtima wanu usamalire njira zanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Chifukwa chake tsono, atero Yehova wa makamu: Mtima wanu usamalire njira zanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 “Nchifukwa chake tsono Ine Chauta Wamphamvuzonse ndikunena kuti muganizepo bwinotu pamenepa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Tsono zimene Yehova Wamphamvuzonse akunena ndi izi, “Ganizirani bwino njira zanu. Onani mutuwo |