Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Hagai 1:5 - Buku Lopatulika

5 Chifukwa chake tsono, atero Yehova wa makamu: Mtima wanu usamalire njira zanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Chifukwa chake tsono, atero Yehova wa makamu: Mtima wanu usamalire njira zanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 “Nchifukwa chake tsono Ine Chauta Wamphamvuzonse ndikunena kuti muganizepo bwinotu pamenepa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Tsono zimene Yehova Wamphamvuzonse akunena ndi izi, “Ganizirani bwino njira zanu.

Onani mutuwo Koperani




Hagai 1:5
15 Mawu Ofanana  

Penyetsetsani malinga ake, yesetsani zinyumba zake; kuti mukaziwerengere mibadwo ikudza m'mbuyo.


Ndipo Farao anatembenuka, nalowa m'nyumba yake, osasamalira ichi chomwe mumtima mwake.


koma iyeyu wosasamalira mau a Yehova anasiya anyamata ndi zoweta zake kubusa.


Tisanthule ntiyese njira zathu ntibwerenso kwa Yehova.


Popeza anasamalira, natembenukira kuleka zolakwa zake zonse adazichita, adzakhala ndi moyo ndithu, sadzafa.


Ndipo munthuyu anati kwa ine, Wobadwa ndi munthu iwe, penya ndi maso ako, imva m'makutu mwako, nuike mtima wako pa zonse ndidzakuonetsa iwe; pakuti unatengedwa kudza kuno, kuti ndikuonetse izi; fotokozera nyumba ya Israele zonse uziona.


Pamenepo anati kwa ine, Usaope Daniele; pakuti kuyambira tsiku loyamba lija unaika mtima wako kuzindikira ndi kudzichepetsa pamaso pa Mulungu wako, mau ako anamveka; ndipo ndadzera mau ako.


Ndipo mfumu m'mene atamva mau awa anaipidwa kwambiri, naika mtima wake pa Daniele kuti amlanditse, nayesetsa mpaka polowa dzuwa kumlanditsa.


Kodi imeneyi ndiyo nthawi yakuti inu nokha mukhala m'nyumba zanu zochingidwa m'katimo, ndi nyumba iyi ikhale yopasuka?


Mwabzala zambiri, koma mututa pang'ono; mukudya, koma osakhuta; mukumwa, koma osakoledwa; mudziveka, koma palibe wofundidwa; ndi iye wolembedwa ntchito yakulipidwa alandirira kulipirako m'thumba lobooka.


Atero Yehova wa makamu: Mtima wanu usamalire njira zanu.


Koma m'mene anakumbukira mumtima, anati, Antchito olipidwa ambiri a atate wanga ali nacho chakudya chochuluka, ndipo ine ndionongeke kuno ndi njala?


Dziyeseni nokha, ngati muli m'chikhulupiriro, dzitsimikizeni nokha. Kapena simuzindikira kodi za inu nokha kuti Yesu Khristu ali mwa inu? Mukapanda kukhala osatsimikizidwa.


Koma yense ayesere ntchito yake ya iye yekha, ndipo pamenepo adzakhala nako kudzitamandira chifukwa cha iye yekha, si chifukwa cha wina.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa