Hagai 1:12 - Buku Lopatulika12 Pamenepo Zerubabele mwana wa Sealatiele, ndi Yoswa mwana wa Yehozadaki, mkulu wa ansembe, ndi otsala onse a anthu, anamvera mau a Yehova Mulungu wao, ndi mau a Hagai mneneri, monga Yehova Mulungu wao adamtuma; ndipo anthu anaopa pamaso pa Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Pamenepo Zerubabele mwana wa Sealatiele, ndi Yoswa mwana wa Yehozadaki, mkulu wa ansembe, ndi otsala onse a anthu, anamvera mau a Yehova Mulungu wao, ndi mau a Hagai mneneri, monga Yehova Mulungu wao adamtuma; ndipo anthu anaopa pamaso pa Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Pamenepo Zerubabele mwana wa Salatiyele, Yoswa mwana wa Yehozadaki mkulu wa ansembe, ndi anthu ena onse obwerako ku ukapolo, adachita zimene Chauta Mulungu wao adanena. Adamva mau a mneneri Hagai amene Chauta adamtuma, ndipo adachita mantha kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Pamenepo Zerubabeli mwana wa Sealatieli, mkulu wa ansembe Yoswa mwana wa Yehozadaki, ndi anthu onse otsala anamvera mawu a Yehova Mulungu wawo ndi uthenga wa Hagai, chifukwa anatumidwa ndi Yehova Mulungu wawo. Ndipo anthuwo anaopa Yehova. Onani mutuwo |