Hagai 1:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo ndinaitana chilala chidzere dziko, ndi mapiri, ndi tirigu, ndi vinyo, ndi mafuta, ndi zimene ibala nthaka, ndi anthu, ndi zoweta, ndi ntchito zonse za manja. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo ndinaitana chilala chidzere dziko, ndi mapiri, ndi tirigu, ndi vinyo, ndi mafuta, ndi zimene ibala nthaka, ndi anthu, ndi zoweta, ndi ntchito zonse za manja. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Nkuwonanso ndagwetsa chilala pa dziko lonse, pa minda ya tirigu, ya mphesa ndi ya mitengo ya olivi, pa zonse zomera pa nthaka, ndi pa zonse zimene anthu amalima, ndiponso pa anthu ndi nyama zomwe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Ndabweretsa chilala pa minda ndi pa mapiri, chilala chawumitsa tirigu, mphesa, mafuta a olivi ndi chilichonse chimene chimamera pa nthaka, pa anthu ndi pa ngʼombe, ndi pa ntchito zonse za manja anu.” Onani mutuwo |