Hagai 1:10 - Buku Lopatulika10 M'mwemo chifukwa cha inu kumwamba kukaniza mame, ndi nthaka ikaniza zipatso zake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 M'mwemo chifukwa cha inu kumwamba kukaniza mame, ndi nthaka ikaniza zipatso zake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Nkuwonatu mvula yati zii, nthaka yati gwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Choncho, chifukwa cha inu, mitambo yaleka kugwetsa mvula ndipo dziko lapansi laleka kutulutsa zomera. Onani mutuwo |