Genesis 46:32 - Buku Lopatulika32 ndipo anthuwo ali abusa chifukwa anakhala oweta ng'ombe; ndipo anadza ndi nkhosa zao ndi ng'ombe zao ndi zonse ali nazo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 ndipo anthuwo ali abusa chifukwa anakhala oweta ng'ombe; ndipo anadza ndi nkhosa zao ndi ng'ombe zao ndi zonse ali nazo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Anthu ameneŵa ndi abusa, amaŵeta zoŵeta. Nkhosa zao ndi ng'ombe zomwe abwera nazo, pamodzi ndi zinthu zao zonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Anthuwa ndi abusa; amaweta ziweto zawo ndipo abwera ndi nkhosa ndi ngʼombe zawo, pamodzi ndi antchito awo.’ Onani mutuwo |