Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 46:31 - Buku Lopatulika

31 Ndipo Yosefe anati kwa abale ake, ndi kwa mbumba ya atate wake, Ndidzanka, ndikauze Farao, ndipo ndidzati kwa iye, Abale anga ndi mbumba ya atate wanga, amene anali m'dziko la Kanani, afika kwa ine;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 Ndipo Yosefe anati kwa abale ake, ndi kwa mbumba ya atate wake, Ndidzanka, ndikauze Farao, ndipo ndidzati kwa iye, Abale anga ndi mbumba ya atate wanga, amene anali m'dziko la Kanani, afika kwa ine;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

31 Apo Yosefe adauza abale ake aja pamodzi ndi banja lonse la bambo wake kuti “Ndipita ndikamuuze Farao kuti abale anga pamodzi ndi onse a m'banja la atate anga amene ankakhala ku Kanani, abwera kuno kwa ine.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 Ndipo Yosefe anati kwa abale ake pamodzi ndi a pa banja la abambo ake, “Ndipita kwa Farao ndipo ndikamuwuza kuti, ‘Abale anga pamodzi ndi onse a mʼnyumba ya abambo anga amene amakhala mʼdziko la Kanaani abwera kuno kwa ine.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 46:31
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Israele anati kwa Yosefe, Ndife tsopano, popeza ndaona nkhope yako, kuti ukali ndi moyo.


ndipo anthuwo ali abusa chifukwa anakhala oweta ng'ombe; ndipo anadza ndi nkhosa zao ndi ng'ombe zao ndi zonse ali nazo.


ndipo popeza anali wa ntchito imodzimodzi, anakhala nao, ndipo iwowa anagwira ntchito; pakuti ntchito yao inali yakusoka mahema.


Pakuti Iye wakuyeretsa ndi iwo akuyeretsedwa achokera onse mwa mmodzi; chifukwa cha ichi alibe manyazi kuwatcha iwo abale.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa