Genesis 46:27 - Buku Lopatulika27 ndi ana aamuna a Yosefe, amene anambadwira iye mu Ejipito ndiwo anthu awiri; anthu onse a mbumba ya Yakobo, amene analowa mu Ejipito anali makumi asanu ndi awiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 ndi ana amuna a Yosefe, amene anambadwira iye m'Ejipito ndiwo anthu awiri; anthu onse a mbumba ya Yakobo, amene analowa m'Ejipito anali makumi asanu ndi awiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Popeza kuti Yosefe adaabereka ana aŵiri ku Ejipito, chiŵerengero chidafika 70. Onseŵa anali a m'banja la Yakobe, ndipo ndiwo adapita ku Ejipito. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Pophatikiza ana awiri a Yosefe obadwira ku Igupto, anthu a pa banja la Yakobo amene anapita ku Igupto, onse pamodzi analipo 70. Onani mutuwo |