Genesis 46:26 - Buku Lopatulika26 Ndi anthu onse amene anadza ndi Yakobo mu Ejipito, amene anatuluka m'chuuno mwake, pamodzi ndi akazi a ana aamuna a Yakobo ndiwo makumi asanu ndi limodzi kudza asanu ndi mmodzi; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Ndi anthu onse amene anadza ndi Yakobo m'Ejipito, amene anatuluka m'chuuno mwake, pamodzi ndi akazi a ana amuna a Yakobo ndiwo makumi asanu ndi limodzi kudza asanu ndi mmodzi; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Chiŵerengero chonse cha anthu ochokera mwa Yakobe, amene adapita ku Ejipito, chinali 66, osaŵerengera akazi a ana ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Onse amene anapita ndi Yakobo (iwo amene anali akeake, osawerengera akazi a ana ake), analipo 66. Onani mutuwo |