Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 46:25 - Buku Lopatulika

25 Amenewa ndi ana a Biliha, amene Labani anampatsa Rakele mwana wake wamkazi, amenewo anambalira Yakobo; anthu onse ndiwo asanu ndi awiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Amenewa ndi ana a Biliha, amene Labani anampatsa Rakele mwana wake wamkazi, amenewo anambalira Yakobo; anthu onse ndiwo asanu ndi awiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 (Asanu ndi aŵiriŵa ndiwo adzukulu a Yakobe amene adabadwa mwa Biliha, amene Labani adaapereka kwa mwana wake Rakele.)

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Amenewa ndi zidzukulu za Yakobo mwa Biliha amene Labani anapereka kwa mwana wake Rakele. Onse pamodzi analipo asanu ndi awiri.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 46:25
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Labani anampatsa mwana wake wamkazi Rakele Biliha mdzakazi wake kuti akhale mdzakazi wa Rakele.


Ndipo panali pamene Israele anakhala m'dzikomo, Rubeni anamuka nagona ndi Biliha, mkazi wamng'ono wa atate wake: ndipo Israele anamva. Ana aamuna a Yakobo anali khumi ndi awiri:


ana aamuna a Biliha mdzakazi wake wa Rakele: ndiwo Dani ndi Nafutali;


Ndi ana aamuna a Nafutali: Yazeele, ndi Guni, ndi Yezere ndi Silemu.


Rubeni, Simeoni, Levi ndi Yuda;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa