Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 46:22 - Buku Lopatulika

22 Amenewo ndi ana a Rakele, amene anabadwira Yakobo; anthu onse ndiwo khumi ndi anai.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Amenewo ndi ana a Rakele, amene anabadwira Yakobo; anthu onse ndiwo khumi ndi anai.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 (Onseŵa 14 ndiwo adzukulu a Yakobe mwa mkazi wake Rakele.)

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Amenewa ndi zidzukulu za Yakobo mwa mkazi wake Rakele. Onse analipo khumi ndi anayi.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 46:22
3 Mawu Ofanana  

Ndipo kapolo wanu atate wanga anati kwa ife, Inu mudziwa kuti mkazi wanga anandibalira ine ana aamuna awiri;


Ndi ana aamuna a Benjamini: Bela ndi Bekere, ndi Asibele, ndi Gera, ndi Naamani, ndi Ehi ndi Rosi, Mupimu ndi Hupimu, ndi Aridi.


Ndi ana aamuna a Dani: Husimu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa