Genesis 46:20 - Buku Lopatulika20 Kwa Yosefe kunabadwa m'dziko la Ejipito Manase ndi Efuremu, amene Asenati mwana wamkazi wa Potifera wansembe wa Oni anambalira iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Kwa Yosefe kunabadwa m'dziko la Ejipito Manase ndi Efuremu, amene Asenati mwana wamkazi wa Potifera wansembe wa Oni anambalira iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Manase ndi Efuremu anali ana amene Yosefe adabereka mwa Asenati, mwana wa Potifera wansembe wa ku Oni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Ku Igupto, Asenati mwana wa Potifara wansembe wa Oni, anamuberekera Yosefe ana awa: Manase ndi Efereimu. Onani mutuwo |