Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 46:19 - Buku Lopatulika

19 Ana a Rakele mkazi wake wa Yakobo: Yosefe ndi Benjamini.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Ana a Rakele mkazi wake wa Yakobo: Yosefe ndi Benjamini.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Ana a Rakele mkazi wa Yakobe anali aŵa: Yosefe ndi Benjamini.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Ana aamuna a Rakele mkazi wa Yakobo anali: Yosefe ndi Benjamini.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 46:19
18 Mawu Ofanana  

Ndipo Yakobo anamkonda Rakele, nati, Ndidzakutumikirani inu zaka zisanu ndi ziwiri chifukwa cha Rakele mwana wanu wamkazi wamng'ono.


namutcha dzina lake Yosefe; ndipo anati, Yehova anandionjezera ine mwana wamwamuna wina.


ana aamuna a Rakele: ndiwo Yosefe ndi Benjamini;


Ndipo anatsika naye Yosefe kunka ku Ejipito; ndipo Potifara, nduna ya Farao, kazembe wa alonda, Mwejipito, anamgula iye m'manja mwa Aismaele amene anatsika naye kunka kumeneko.


Ndipo kapolo wanu atate wanga anati kwa ife, Inu mudziwa kuti mkazi wanga anandibalira ine ana aamuna awiri;


Amenewa ndi ana a Zilipa, amene Labani anampatsa Leya mwana wake wamkazi, amenewo anambalira Yakobo, anthu khumi ndi asanu ndi mmodzi.


Kwa Yosefe kunabadwa m'dziko la Ejipito Manase ndi Efuremu, amene Asenati mwana wamkazi wa Potifera wansembe wa Oni anambalira iye.


Dani, Yosefe, ndi Benjamini, Nafutali, Gadi, ndi Asere.


Isakara, Zebuloni, ndi Benjamini;


Ndipo amoyo onse amene anatuluka m'chuuno mwake mwa Yakobo ndiwo makumi asanu ndi awiri; koma Yosefe anali mu Ejipito.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa