Genesis 46:19 - Buku Lopatulika19 Ana a Rakele mkazi wake wa Yakobo: Yosefe ndi Benjamini. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ana a Rakele mkazi wake wa Yakobo: Yosefe ndi Benjamini. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Ana a Rakele mkazi wa Yakobe anali aŵa: Yosefe ndi Benjamini. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Ana aamuna a Rakele mkazi wa Yakobo anali: Yosefe ndi Benjamini. Onani mutuwo |