Genesis 46:15 - Buku Lopatulika15 Amenewo ndi ana aamuna a Leya, amene anambalira Yakobo ku Padanaramu, pamodzi ndi mwana wamkazi wake Dina; ana aamuna ndi aakazi onse ndiwo anthu makumi atatu kudza atatu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Amenewo ndi ana amuna a Leya, amene anambalira Yakobo m'Padanaramu, pamodzi ndi mwana wamkazi wake Dina; ana aamuna ndi aakazi onse ndiwo anthu makumi atatu kudza atatu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 (Ana ameneŵa ndiwo amene Leya adabalira Yakobe ku Mesopotamiya kuja, ndipo panalinso mwana wake wamkazi Dina. Adzukulu obadwa mwa Leya analipo 33 onse pamodzi.) Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Amenewa ndi ana aamuna a Leya amene anamubalira Yakobo ku Padanaramu. Panali mwana wamkazi dzina lake Dina. Ana onse analipo 33. Onani mutuwo |