Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 46:14 - Buku Lopatulika

14 Ndi ana aamuna a Zebuloni: Seredi, ndi Eloni ndi Yaleele.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Ndi ana amuna a Zebuloni: Seredi, ndi Eloni ndi Yaleele.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Ana a Zebuloni anali aŵa: Seredi, Eloni ndi Yaleele.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Ana aamuna a Zebuloni ndi awa: Seredi, Eloni ndi Yahaleeli.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 46:14
9 Mawu Ofanana  

Ndi ana aamuna a Isakara: Tola ndi Puva, ndi Iyobu, ndi Simironi.


Amenewo ndi ana aamuna a Leya, amene anambalira Yakobo ku Padanaramu, pamodzi ndi mwana wamkazi wake Dina; ana aamuna ndi aakazi onse ndiwo anthu makumi atatu kudza atatu.


Zebuloni adzakhala m'mphepete mwa nyanja; ndipo iye adzakhala dooko la ngalawa; ndipo malire ake adakhala pa Sidoni.


Ana a Israele ndi awa: Rubeni, Simeoni, Levi, ndi Yuda, Isakara, ndi Zebuloni,


Wa Zebuloni, Eliyabu mwana wa Heloni.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa