Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 45:28 - Buku Lopatulika

28 ndipo Israele anati, Chakwana; Yosefe mwana wanga akali ndi moyo; ndidzamuka ndikamuone iye ndisanafe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

28 ndipo Israele anati, Chakwana; Yosefe mwana wanga akali ndi moyo; ndidzamuka ndikamuone iye ndisanafe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

28 Tsono adati, “Basi chabwino, mwana wanga Yosefe akali moyo. Ndipita ndikamuwone ndisanafe.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

28 Ndipo Israeli anati, “Ndatsimikizadi! Mwana wanga Yosefe akanali ndi moyodi. Ndipita ndikamuone ndisanafe.”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 45:28
5 Mawu Ofanana  

Ndipo anamfotokozera iye mau onse a Yosefe amene ananena ndi iwo; ndipo pamene anaona magaleta amene Yosefe anatumiza kuti amtengeremo, mtima wa Yakobo atate wao unatsitsimuka;


Ndipo Israele anamuka ulendo wake ndi zonse anali nazo, nafika ku Beereseba, napereka nsembe kwa Mulungu wa Isaki atate wake.


Ndipo Israele anati kwa Yosefe, Ndife tsopano, popeza ndaona nkhope yako, kuti ukali ndi moyo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa