Genesis 44:31 - Buku Lopatulika31 kudzakhala pakuona kuti mnyamatayo palibe, adzafa; ndipo akapolo anu adzamtsitsira ndi chisoni imvi za atate wathu kumanda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 kudzakhala pakuona kuti mnyamatayo palibe, adzafa; ndipo akapolo anu adzamtsitsira ndi chisoni imvi za atate wathu kumanda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 akakangoona kuti iyeyu palibe, basitu akafa. Ndiye kuti ifeyo ndi amene tidzachititse bambo wathu chisoni chofa nacho mu ukalamba wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 ndipo akakaona kuti mnyamatayu palibe, basi akafa. Ife tidzakhala ngati takankhira abambo athu ku manda ndi chisoni. Onani mutuwo |