Genesis 44:30 - Buku Lopatulika30 Chifukwa chake ndikafika kwa kapolo wanu atate wanga, ndipo mnyamata akapanda kukhala ndi ife; popeza moyo wanu uli womangidwa ndi moyo wa mnyamatayo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Chifukwa chake ndikafika kwa kapolo wanu atate wanga, ndipo mnyamata akapanda kukhala ndi ife; popeza moyo wanu uli womangidwa ndi moyo wa mnyamatayo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Yuda adapitiriza kulankhula nati, “Nchifukwa chake tsopano ndikabwerera kwathu kwa bambo wanga, mtumiki wanu, opanda mnyamata ameneyu, amene moyo wa bambo wanga uli pa iye, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 “Tsono ngati tizibwerera kwa mtumiki wanu, abambo athu popanda mnyamatayu, amene moyo wa abambo ake uli pa iyeyu, Onani mutuwo |