Genesis 44:27 - Buku Lopatulika27 Ndipo kapolo wanu atate wanga anati kwa ife, Inu mudziwa kuti mkazi wanga anandibalira ine ana aamuna awiri; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Ndipo kapolo wanu atate wanga anati kwa ife, Inu mudziwa kuti mkazi wanga anandibalira ine ana amuna awiri; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Koma bambo wathu adati, ‘Mukudziŵa kuti mkazi wanga adandibalira ana aŵiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 “Koma kapolo wanu, abambo athu anatiwuza kuti, ‘Inu mukudziwa kuti mkazi wanga anandiberekera ana aamuna awiri. Onani mutuwo |