Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 44:27 - Buku Lopatulika

27 Ndipo kapolo wanu atate wanga anati kwa ife, Inu mudziwa kuti mkazi wanga anandibalira ine ana aamuna awiri;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 Ndipo kapolo wanu atate wanga anati kwa ife, Inu mudziwa kuti mkazi wanga anandibalira ine ana amuna awiri;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

27 Koma bambo wathu adati, ‘Mukudziŵa kuti mkazi wanga adandibalira ana aŵiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 “Koma kapolo wanu, abambo athu anatiwuza kuti, ‘Inu mukudziwa kuti mkazi wanga anandiberekera ana aamuna awiri.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 44:27
8 Mawu Ofanana  

Yakobo ndipo anachita chotero namaliza sabata lake; ndipo Labani anampatsa iye Rakele mwana wake wamkazi kuti akwatire iyenso.


Ndipo iye anati, Mwana wanga sadzatsikira ndi inu, chifukwa kuti mkulu wake wafa, ndipo watsala iye yekha; ngati choipa chikamgwera iye m'njira m'mene mupitamo, inu mudzatsitsira ndi chisoni imvi zanga kumanda.


Ndipo ife tinati, Sitingathe kupita; mphwathu wamng'ono akakhala ndi ife, pamenepo tidzapita; pakuti sitingaone nkhope ya munthu uja, mphwathu wamng'ono akapanda kukhala ndi ife.


Ana a Rakele mkazi wake wa Yakobo: Yosefe ndi Benjamini.


Amenewo ndi ana a Rakele, amene anabadwira Yakobo; anthu onse ndiwo khumi ndi anai.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa