Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 44:24 - Buku Lopatulika

24 Ndipo panali titakwera kunka kwa kapolo wanu atate wanga, tinamfotokozera iye mau a mbuyanga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Ndipo panali titakwera kunka kwa kapolo wanu atate wanga, tinamfotokozera iye mau a mbuyanga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Titabwerera kwathu kwa bambo wathu mtumiki wanu, tidamuuza mau anu onse aja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Ndiye pamene tinafika kwa kapolo wanu, abambo athu tinawawuza zonse zimene munanena.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 44:24
3 Mawu Ofanana  

Ndipo munati kwa akapolo anu, Koma ngati mbale wanu safika pamodzi ndi inu, simudzaonanso konse nkhope yanga.


Ndipo atate wathu anati, Mupitenso mutigulire ife chakudya pang'ono.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa