Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 44:23 - Buku Lopatulika

23 Ndipo munati kwa akapolo anu, Koma ngati mbale wanu safika pamodzi ndi inu, simudzaonanso konse nkhope yanga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Ndipo munati kwa akapolo anu, Koma ngati mbale wanu safika pamodzi ndi inu, simudzaonanso konse nkhope yanga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Tsono paja mudaanena kuti simudzatilola kufikanso pamaso panu tikadzapanda kubwera naye mng'ono wathuyo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Koma inu munatichenjeza kuti, ‘Pokhapokha mutabwera naye mʼbale wanu wamngʼono kwambiri, simudzandionanso.’

Onani mutuwo Koperani




Genesis 44:23
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Yuda ananena ndi iye kuti, Munthu uja anatilimbitsira mau kuti, simudzaonanso nkhope yanga, koma mphwanu akhale ndi inu ndiko.


Koma mukapanda kumtuma iye sititsika; pakuti munthu uja anati kwa ife, Simudzaona nkhope yanga, ngati mphwanu sali ndi inu.


Ndipo ife tinati kwa mbuyanga, Mnyamata sangathei kumsiya atate wake; pakuti akamsiya atate wake, atate wake adzafa.


Ndipo panali titakwera kunka kwa kapolo wanu atate wanga, tinamfotokozera iye mau a mbuyanga.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa