Genesis 44:22 - Buku Lopatulika22 Ndipo ife tinati kwa mbuyanga, Mnyamata sangathei kumsiya atate wake; pakuti akamsiya atate wake, atate wake adzafa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo ife tinati kwa mbuyanga, Mnyamata sangathei kumsiya atate wake; pakuti akamsiya atate wake, atate wake adzafa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Ife tidaakuyankhani kuti, ‘Mnyamatayo sangachoke kwa bambo wake, popeza kuti akatero, bambo wakeyo kufa kudzakhala komweko.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Ife tinati, ‘Mbuye wathu, mnyamatayo sangasiye abambo ake, akawasiya ndiye kuti abambo akewo adzafa.’ Onani mutuwo |