Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 44:21 - Buku Lopatulika

21 Ndipo munati kwa akapolo anu, Munditengere iye, kuti ndimuone iye m'maso mwanga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Ndipo munati kwa akapolo anu, Munditengere iye, kuti ndimuone iye m'maso mwanga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Bwana, paja inu mudaatiwuza kuti, ‘Mudzabwere naye, kuti ndidzamuwone.’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 “Ndipo inu munatiwuza kuti, ‘Mubwere naye kwa ine kuti ndidzamuone ndekha.’

Onani mutuwo Koperani




Genesis 44:21
7 Mawu Ofanana  

Mudzayesedwa ndi ichi, pali moyo wa Farao, simudzatuluka muno, koma akadze kuno mphwanu ndiko.


koma mukatenge mphwanu kudza naye kwa ine, kuti atsimikizidwe mau anu ndipo simudzafa. Ndipo anachita chomwecho.


Ndipo iye anatukula maso ake naona Benjamini mphwake, mwana wa amake, nati, Kodi uyu ndi mphwanu wamng'ono uja, amene munanena ndi ine uja? Ndipo iye anati, Mulungu akuchitire iwe ufulu, mwana wanga.


Ndipo ife tinati kwa mbuyanga, Mnyamata sangathei kumsiya atate wake; pakuti akamsiya atate wake, atate wake adzafa.


Pakuti ndidzaika maso anga pa iwo kuti ndiwachitire iwo bwino, ndipo ndidzawabwezanso kudziko ili: ndipo ndidzamangitsa mudzi wao, osawapasula; ndi kuwabzala, osawazula iwo.


Ndipo tsopano, taona, ndikumasula iwe lero maunyolo ali pa manja ako. Kukakukomera kudza nane ku Babiloni, idza, ndipo ndidzakusamalira bwino; koma kukakuipira kudza nane ku Babiloni, tsala; taona, dziko lonse lili pamaso pako; kulikonse ukuyesa kwabwino kapena koyenera kupitako, pita kumeneko.


Angakhale alowa ndende pamaso pa adani ao, kumeneko ndidzalamulira lupanga, ndipo lidzawapha; ndipo ndidzayang'anitsa maso anga kwa iwowa, kuwachitira choipa, si chokoma ai.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa