Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 44:19 - Buku Lopatulika

19 Mbuyanga anafunsa akapolo ake kuti, Kodi muli ndi atate wanu kapena mbale wanu?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Mbuyanga anafunsa akapolo ake kuti, Kodi muli ndi atate wanu kapena mbale wanu?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Bwana, paja mudaatifunsa kuti, ‘Kodi muli naye bambo wanu kapena mbale wanu?’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Mbuye wanga munafunsa akapolo anufe kuti, ‘Kodi muli ndi abambo anu kapena mʼbale wanu?’

Onani mutuwo Koperani




Genesis 44:19
4 Mawu Ofanana  

Ndipo iye anatukula maso ake naona Benjamini mphwake, mwana wa amake, nati, Kodi uyu ndi mphwanu wamng'ono uja, amene munanena ndi ine uja? Ndipo iye anati, Mulungu akuchitire iwe ufulu, mwana wanga.


Ndipo iwo anati, Munthuyo anafunsitsa za ife, ndi za abale athu, kuti, Atate wanu alipo? Kodi muli ndi mphwanu? Ndipo tinamfotokozera iye monga mwa mau amenewo: ngati tinadziwa kuti iye adzati, Idzani naye mphwanu?


Ndipo tinati kwa mbuyanga, Tili ndi atate, munthu wokalamba, ndi mwana wa ukalamba wake wamng'ono; mbale wake wafa, ndipo iye yekha watsala wa amake, ndipo atate wake amkonda iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa