Genesis 44:19 - Buku Lopatulika19 Mbuyanga anafunsa akapolo ake kuti, Kodi muli ndi atate wanu kapena mbale wanu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Mbuyanga anafunsa akapolo ake kuti, Kodi muli ndi atate wanu kapena mbale wanu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Bwana, paja mudaatifunsa kuti, ‘Kodi muli naye bambo wanu kapena mbale wanu?’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Mbuye wanga munafunsa akapolo anufe kuti, ‘Kodi muli ndi abambo anu kapena mʼbale wanu?’ Onani mutuwo |