Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 43:31 - Buku Lopatulika

31 Ndipo anasamba nkhope yake, natuluka; ndipo anadziletsa, nati, Ikani chakudya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 Ndipo anasamba nkhope yake, natuluka; ndipo anadziletsa, nati, Ikani chakudya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

31 Atapukuta m'maso adatuluka, ndipo adalimbanso mtima, nalamula kuti chakudya chibwere.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 Atatha kupukuta misozi mʼmaso mwake anatuluka, ndipo modzilimbitsa analamula kuti chakudya chibwere.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 43:31
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Yosefe sanakhoze kudziletsa pamaso pa onse amene anaima naye: nati, Tulutsa anthu onse pamaso panga. Ndipo panalibe munthu pamodzi ndi iye pamene Yosefe anadziululira yekha kwa abale ake.


Pochuluka mau zolakwa sizisoweka; koma wokhala chete achita mwanzeru.


Ndakhala nthawi yambiri wosalankhula ndakhala chete kudzithungata ndekha; tsopano ndidzafuula ngati mkazi wobala; ndidzapuma modukizadukiza ndi wefuwefu pamodzi.


Yehova atero: Letsa mau ako asalire, ndi maso anu asagwe misozi; pakuti ntchito yako idzalandira mphotho, ati Yehova; ndipo adzabweranso kuchokera kudziko la mdani.


Pakuti, Iye wofuna kukonda moyo, ndi kuona masiku abwino, aletse lilime lake lisanene choipa, ndi milomo yake isalankhule chinyengo;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa