Genesis 43:31 - Buku Lopatulika31 Ndipo anasamba nkhope yake, natuluka; ndipo anadziletsa, nati, Ikani chakudya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Ndipo anasamba nkhope yake, natuluka; ndipo anadziletsa, nati, Ikani chakudya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Atapukuta m'maso adatuluka, ndipo adalimbanso mtima, nalamula kuti chakudya chibwere. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Atatha kupukuta misozi mʼmaso mwake anatuluka, ndipo modzilimbitsa analamula kuti chakudya chibwere. Onani mutuwo |