Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 36:32 - Buku Lopatulika

32 Ndipo Bela mwana wamwamuna wa Beori, analamulira mu Edomu, ndipo dzina la mzinda wake ndilo Dinihaba.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

32 Ndipo Bela mwana wamwamuna wa Beori, analamulira m'Edomu, ndipo dzina la mudzi wake ndilo Dinihaba.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

32 Bela mwana wa Beori, ankalamulira dziko la Edomu, ndipo dzina la mzinda wake linali Dinihaba.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

32 Bela mwana wa Beori anakhala mfumu ya ku Edomu. Mzinda wake ankawutcha Dinihaba.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 36:32
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Bela anamwalira, ndipo Yobabu mwana wamwamuna wa Zera wa ku Bozira analamulira m'malo mwake.


Mafumu tsono akuchita ufumu m'dziko la Edomu, pakalibe mfumu wakuchita ufumu pa ana a Israele, ndiwo Bela mwana wa Beori; ndi dzina la mzinda wake ndilo Dinihaba.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa