Genesis 36:31 - Buku Lopatulika31 Amenewa ndi mafumu analamulira m'dziko la Edomu, asadalamulire ana a Israele mfumu aliyense. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Amenewa ndi mafumu analamulira m'dziko la Edomu, asadalamulire ana a Israele mfumu aliyense. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Naŵa mafumu amene ankalamulira dziko la Edomu, mafumu a Aisraele asanayambe kulamulira kumeneko: Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Awa ndi mafumu amene ankalamulira dziko la Edomu, mfumu iliyonse ya Israeli isanayambe kulamulira kumeneko: Onani mutuwo |