Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 36:29 - Buku Lopatulika

29 Mafumu obadwa kwa Ahori: mfumu Lotani, mfumu Sobala, mfumu Zibiyoni, mfumu Ana,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

29 Mafumu obadwa kwa Ahori: mfumu Lotani, mfumu Sobala, mfumu Zibiyoni, mfumu Ana,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

29 Mafumu a Ahori ndi aŵa: Lotani, Sobali, Zibiyoni, Ana,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

29 Mafumu a Ahori anali awa: Lotani, Sobala, Zibeoni, Ana,

Onani mutuwo Koperani




Genesis 36:29
6 Mawu Ofanana  

Esau anatenga akazi ake a ana aakazi a mu Kanani: Ada mwana wamkazi wa Eloni Muhiti, ndi Oholibama mwana wamkazi wa Ana, mwana wamkazi wa Zibiyoni Muhivi;


Amenewa ndi ana aamuna a Seiri Muhori, okhala m'dzikomo: Lotani ndi Sobala, ndi Zibiyoni, ndi Ana,


Ana a Disani ndi awa: Uzi ndi Arani.


mfumu Disoni, mfumu Ezere, mfumu Disani; amenewa ndi mafumu obadwa kwa Ahori, monga mwa maufumu ao m'dziko la Seiri.


Ndi ana a Seiri: Lotani, ndi Sobala, ndi Zibiyoni, ndi Ana, ndi Disoni, ndi Ezere, ndi Disani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa