Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 36:22 - Buku Lopatulika

22 Ndi ana a Lotani anali Hori ndi Hemani: mlongo wake wa Lotani anali Timna.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Ndi ana a Lotani anali Hori ndi Hemani: mlongo wake wa Lotani anali Timna.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Ana a Lotani anali Hori ndi Hemani, ndipo Timna anali mlongo wa Lotani.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Ana aamuna a Lotani anali awa: Hori ndi Homamu. Timna anali mlongo wake wa Lotani.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 36:22
3 Mawu Ofanana  

ndi Disoni ndi Ezere ndi Disani; amenewa ndi mafumu obadwa kwa Ahori, ana a Seiri, m'dziko la Edomu.


Ana a Sobala ndi awa: Alivani ndi Manahati ndi Ebala, Sefo ndi Onamu.


Ndi ana a Lotani: Hori, ndi Homamu; ndipo Timna ndiye mlongo wake wa Lotani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa