Genesis 35:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo anafa Debora mlezi wa Rebeka, naikidwa kunsi kwa Betele, pansi pa mtengo wathundu; ndipo anatcha dzina lake Aloni-Bakuti. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo anafa Debora mlezi wa Rebeka, naikidwa kunsi kwa Betele, pansi pa mtengo wathundu; ndipo anatcha dzina lake Aloni-Bakuti. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Debora mlezi wa Rakele, adamwalira komweko, ndipo adaikidwa patsinde pa mtengo wathundu ku Beteleko. Motero malowo adatchedwa Mtengo Wamaliro. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Debora mlezi wa Rakele anamwalira komweko nayikidwa mʼmanda pansi pa mtengo wa thundu cha kumunsi kwa Beteli. Choncho panatchedwa Aloni-Bakuti (mtengo wamaliro). Onani mutuwo |