Genesis 35:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo Yakobo anafika ku Luzi, ndiko ku dziko la Kanani (ndiwo Betele), iye ndi anthu onse anali pamodzi ndi iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo Yakobo anafika ku Luzi, ndiko ku dziko la Kanani (ndiwo Betele), iye ndi anthu onse anali pamodzi ndi iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Tsono Yakobe adafika ndi anthu ake ku Luzi (ndiye kuti Betele) m'dziko la Kanani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Yakobo ndi anthu onse anali naye aja anafika ku Luzi (ku Beteli) mu dziko la Kanaani. Onani mutuwo |