Genesis 35:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo anapita ndipo kuopsa kwa Mulungu kudagwera mizinda yakuwazinga, ndipo sanalondole ana a Yakobo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo anapita ndipo kuopsa kwa Mulungu kudagwera midzi yakuwazinga, ndipo sanalondole ana a Yakobo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Pamene Yakobe ndi ana ake adachoka, anthu onse a mizinda yozungulira adachita mantha, motero sadaŵatsatire. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Pamenepo ananyamuka, ndipo mtima woopa Mulungu unagwera anthu onse a mʼmizinda yozungulira, kotero kuti palibe aliyense amene anatsatira banja la Yakobo. Onani mutuwo |