Genesis 35:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo anampatsa Yakobo milungu yachilendo yonse inali m'manja mwao, ndi mphete zinali m'makutu mwao: ndipo Yakobo anazibisa pansi pa mtengo wathundu unali pa Sekemu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo anampatsa Yakobo milungu yachilendo yonse inali m'manja mwao, ndi mphete zinali m'makutu mwao: ndipo Yakobo anazibisa pansi pa mtengo wathundu unali pa Sekemu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Motero milungu yonse yachilendo imene ana ake anali nayo, adaipereka kwa Yakobe, pamodzinso ndi ndolo zakukhutu zimene ankavala. Zonsezo adazifotsera patsinde pa mtengo wa thundu pafupi ndi Sekemu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Choncho anamupatsa Yakobo milungu yachilendo yonse imene anali nayo pamodzi ndi ndolo. Iye anazikwirira pansi pa mtengo wa thundu ku Sekemu. Onani mutuwo |