Genesis 35:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo anachokera ku Betele: ndipo panatsala nthawi asanafike ku Efurata: ndipo Rakele anabala navutidwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo anachokera ku Betele: ndipo panatsala nthawi asanafike ku Efurata: ndipo Rakele anabala navutidwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Tsono onse adachoka ku Betele, koma asanafike ku Efurata, nthaŵi yoti Rakele aone mwana idamukwanira, ndipo kubereka kwake kudamuvuta kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Kenaka anachoka ku Beteli. Koma ali pafupi kufika ku Efurata nthawi yakuti Rakele aone mwana inakwana. Iye anavutika pobereka. Onani mutuwo |