Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 34:31 - Buku Lopatulika

31 Ndipo iwo anati, Kodi iye ayenera kusandutsa mlongo wathu wadama?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 Ndipo iwo anati, Kodi iye ayenera kusandutsa mlongo wathu wadama?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

31 Koma iwowo adati, “Pepani, mlongo wathu sangamusandutse mkazi wachiwerewere ai!”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 Koma iwo anayankha kuti, “Pepani, nanga achite kumusandutsa mlongo wathu ngati mkazi wachiwerewere?”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 34:31
6 Mawu Ofanana  

Ndipo ana ake aamuna a Yakobo anayankha Sekemu ndi Hamori atate wake monyenga, nanena, popeza anamuipitsa Dina mlongo wao,


Ndipo ana aamuna a Yakobo anadza kwa ophedwa nafunkha mzinda chifukwa anamuipitsa mlongo wao.


Ndipo Yakobo anati kwa Simeoni ndi Levi, Mwandisautsa ndi kundinukhitsa ine mwa anthu okhala m'dzikomu, mwa Akanani ndi mwa Aperizi; ndipo ine ndine wa anthu owerengeka, adzandisonkhanira ine ndi kundikantha: ndipo ndidzapasulidwa ine ndi a pa nyumba yanga.


Ndipo Mulungu anati kwa Yakobo, Nyamuka nukwere kunka ku Betele nukhale kumeneko: numange kumeneko guwa la nsembe la Mulungu amene anaonekera kwa iwe pamene unathawa ku nkhope ya Esau mbale wako.


Kutembereredwe kukwiya kwao, chifukwa kunali koopsa; ndi kupsa mtima kwao, chifukwa kunali kwankhalwe. Ndidzawagawanitsa mu Yakobo. Ndidzabalalitsa iwo mu Israele.


Pakuti nsanje ndiyo ukali wa mwamuna, ndipo sadzachitira chifundo tsiku lobwezera chilango.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa