Genesis 34:31 - Buku Lopatulika31 Ndipo iwo anati, Kodi iye ayenera kusandutsa mlongo wathu wadama? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Ndipo iwo anati, Kodi iye ayenera kusandutsa mlongo wathu wadama? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Koma iwowo adati, “Pepani, mlongo wathu sangamusandutse mkazi wachiwerewere ai!” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Koma iwo anayankha kuti, “Pepani, nanga achite kumusandutsa mlongo wathu ngati mkazi wachiwerewere?” Onani mutuwo |