Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 34:29 - Buku Lopatulika

29 ndi chuma chao chonse ndi ana ao ndi akazi ao anawagwira, nafunkha zonse za m'nyumba.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

29 ndi chuma chao chonse ndi ana ao ndi akazi ao anawagwira, nafunkha zonse za m'nyumba.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

29 Adatenga chuma chonse, nagwira akazi onse ndi ana, nkutenganso zonse za m'nyumba mwao.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

29 Anawatengera chuma chawo chonse, akazi ndi ana awo, pamodzi ndi zonse zimene zinapezeka mʼnyumba zawo. Zonsezi zinayesedwa ngati zolandidwa ku nkhondo.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 34:29
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Labani anati kwa Yakobo, Wachitanji? Wathawa kwa ine mobisika ndi kutenga ana anga aakazi, monga mikoli ya lupanga.


Ndipo ana aamuna a Yakobo anadza kwa ophedwa nafunkha mzinda chifukwa anamuipitsa mlongo wao.


Ndipo analanda nkhosa zao ndi zoweta zao ndi abulu ao, ndi za m'mzinda, ndi za m'munda;


Ndipo Yakobo anati kwa Simeoni ndi Levi, Mwandisautsa ndi kundinukhitsa ine mwa anthu okhala m'dzikomu, mwa Akanani ndi mwa Aperizi; ndipo ine ndine wa anthu owerengeka, adzandisonkhanira ine ndi kundikantha: ndipo ndidzapasulidwa ine ndi a pa nyumba yanga.


Ndipo anapita nazo zofunkha zonse, ndi zakunkhondo zonse, ndizo anthu ndi nyama.


Ndipo ana a Israele anagwira akazi a Amidiyani, ndi ana aang'ono, nafunkha ng'ombe zao zonse, ndi zoweta zao zonse, ndi chuma chao chonse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa